Site icon Treasure Hymns – Chichewa

Hymn 414 INU bambo, inu mayi,

Chichewa Christian Hymns

Hymn 414 INU bambo, inu mayi,

 

INU bambo, inu mayi,
M’tsateni Mbuye m’tsateni;
Adziwa zinsinsi zanu,
M’tsateni Mbuye m’tsateni.

Anapeza mavutowo,
Napereka moyo wake,
Namwa ndulu m’malo mwathu;
M’tsateni Mbuye m’tsateni.

Anyamata, atsikana,
M’tsateni Mbuye m’tsateni;
Adziwa zinsinsi zanu,
M’tsateni Mbuye m’tsateni.

Anthu onse a padziko,
M’tsateni Mbuye m’tsateni;
Adziwa zinsinsi zanu,
M’tsateni Mbuye m’tsateni.

Exit mobile version