Site icon Treasure Hymns – Chichewa

Hymn 870 Satana apambana tikayamba kusiyana;

Chichewa Believers Christian Hymns

Hymn 870 Satana apambana tikayamba kusiyana;

 

Satana apambana tikayamba kusiyana;

Tikayanjana, yemwe adzagonja ndi kuthawa;

Mbuyathu adzamthyola konse ndi kumlamulira.

Tiyeni tonse, m’Mpingo ‘modzi tiziyenderana.

Exit mobile version