Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 870 Satana apambana tikayamba kusiyana;
Satana apambana tikayamba kusiyana;
Tikayanjana, yemwe adzagonja ndi kuthawa;
Mbuyathu adzamthyola konse ndi kumlamulira.
Tiyeni tonse, m’Mpingo ‘modzi tiziyenderana.
Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 870 Satana apambana tikayamba kusiyana;
Satana apambana tikayamba kusiyana;
Tikayanjana, yemwe adzagonja ndi kuthawa;
Mbuyathu adzamthyola konse ndi kumlamulira.
Tiyeni tonse, m’Mpingo ‘modzi tiziyenderana.