{"id":4060,"date":"2025-12-14T12:43:30","date_gmt":"2025-12-14T12:43:30","guid":{"rendered":"https:\/\/treasurehymns.com\/nya\/2025\/12\/14\/hymn-335-kwathu-sipadziko-ndingopitilira\/"},"modified":"2025-12-14T12:43:30","modified_gmt":"2025-12-14T12:43:30","slug":"hymn-335-kwathu-sipadziko-ndingopitilira","status":"publish","type":"post","link":"https:\/\/treasurehymns.com\/nya\/chichewa-christian-hymns\/hymn-335-kwathu-sipadziko-ndingopitilira\/","title":{"rendered":"Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,"},"content":{"rendered":"<h2>Chichewa Christian Hymns<\/h2>\n<h2>Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira,<\/h2>\n<p>&nbsp;<\/p>\n<p>KWATHU sipadziko, ndingopitilira,<br \/>\nNdadzikundikira chuma Kumwambako;<br \/>\nMngelo akodola pakhomo la M&#8217;mwamba,<br \/>\nNdipo dziko lapansi sindiyesa kwathu.<\/p>\n<p>Mbuye, ndi &#8216;Nu Bwenzi langa ndithu.<br \/>\nNdichitenji ngati Kumwamba sikwathu?<br \/>\nMngelo akodola pakhomo la M&#8217;mwamba,<br \/>\nNdipo dziko lapansi sindiyesa kwathu.<\/p>\n<p>Andiyembekeza, chinthuchi ndidziwa,<br \/>\nMpulumutsi wanga wandikhu&#8217;lukira;<br \/>\nAdzandipyoletsa pamene ndafoka,<br \/>\nNdipo dziko lapansi sindiyesa kwathu.<\/p>\n<p>Mbuye watsogola ku Ulemerero,<br \/>\nNdifuna kugwira dzanja lake konko;<br \/>\nAndidikiranso pakhomo la M&#8217;mwamba,<br \/>\nNdipo dziko lapansi sindiyesa kwathu.<\/p>\n<p>Mu Ulemelero tidzakhala m&#8217;yaya,<br \/>\nOyera mtimawo ali kulambira;<br \/>\nAti: &#8220;Aleluya kwa Mlungu wamphamvu,&#8221;<br \/>\nNdipo dziko lapansi sindiyesa kwathu<\/p>\n","protected":false},"excerpt":{"rendered":"<p>Chichewa Christian Hymns Hymn 335 KWATHU sipadziko, ndingopitilira, &nbsp; KWATHU sipadziko, ndingopitilira, Ndadzikundikira chuma Kumwambako; Mngelo akodola pakhomo la M&#8217;mwamba, Ndipo dziko lapansi sindiyesa kwathu. Mbuye, ndi &#8216;Nu Bwenzi langa ndithu. Ndichitenji ngati Kumwamba sikwathu? Mngelo akodola pakhomo la M&#8217;mwamba, Ndipo dziko lapansi sindiyesa kwathu. Andiyembekeza, chinthuchi ndidziwa, Mpulumutsi wanga wandikhu&#8217;lukira; Adzandipyoletsa pamene ndafoka, Ndipo [&hellip;]<\/p>\n","protected":false},"author":1,"featured_media":0,"comment_status":"open","ping_status":"open","sticky":false,"template":"","format":"standard","meta":{"footnotes":""},"categories":[115],"tags":[],"class_list":["post-4060","post","type-post","status-publish","format-standard","hentry","category-chichewa-christian-hymns"],"amp_enabled":true,"_links":{"self":[{"href":"https:\/\/treasurehymns.com\/nya\/wp-json\/wp\/v2\/posts\/4060","targetHints":{"allow":["GET"]}}],"collection":[{"href":"https:\/\/treasurehymns.com\/nya\/wp-json\/wp\/v2\/posts"}],"about":[{"href":"https:\/\/treasurehymns.com\/nya\/wp-json\/wp\/v2\/types\/post"}],"author":[{"embeddable":true,"href":"https:\/\/treasurehymns.com\/nya\/wp-json\/wp\/v2\/users\/1"}],"replies":[{"embeddable":true,"href":"https:\/\/treasurehymns.com\/nya\/wp-json\/wp\/v2\/comments?post=4060"}],"version-history":[{"count":0,"href":"https:\/\/treasurehymns.com\/nya\/wp-json\/wp\/v2\/posts\/4060\/revisions"}],"wp:attachment":[{"href":"https:\/\/treasurehymns.com\/nya\/wp-json\/wp\/v2\/media?parent=4060"}],"wp:term":[{"taxonomy":"category","embeddable":true,"href":"https:\/\/treasurehymns.com\/nya\/wp-json\/wp\/v2\/categories?post=4060"},{"taxonomy":"post_tag","embeddable":true,"href":"https:\/\/treasurehymns.com\/nya\/wp-json\/wp\/v2\/tags?post=4060"}],"curies":[{"name":"wp","href":"https:\/\/api.w.org\/{rel}","templated":true}]}}