{"id":3753,"date":"2025-12-14T12:42:57","date_gmt":"2025-12-14T12:42:57","guid":{"rendered":"https:\/\/treasurehymns.com\/nya\/2025\/12\/14\/hymn-28-ambuye-ngwodalitsika\/"},"modified":"2025-12-14T12:42:57","modified_gmt":"2025-12-14T12:42:57","slug":"hymn-28-ambuye-ngwodalitsika","status":"publish","type":"post","link":"https:\/\/treasurehymns.com\/nya\/chichewa-christian-hymns\/hymn-28-ambuye-ngwodalitsika\/","title":{"rendered":"Hymn 28 AMBUYE ngwodalitsika,"},"content":{"rendered":"<h2>Chichewa Christian Hymns<\/h2>\n<h2>Hymn 28 AMBUYE ngwodalitsika,<\/h2>\n<p>&nbsp;<\/p>\n<p>AMBUYE ngwodalitsika,<br \/>\nMulungu wa Israyeli ndiye,<br \/>\nPoti anayang\u2019ana na\u0175awombola anthu ake,<\/p>\n<p>Napulumutsa tonse mwapfuko la Davide mwana wake;<br \/>\nMonga analankhula mwa aneneri ake,<\/p>\n<p>Adzatipulumutsa kudzanja la onse akutida,<br \/>\nNdipo adzachitira akulu chifundo ndi chisoni.<\/p>\n<p>Ndiye akumbukira pangani loyera lake lija,<br \/>\nNdi chilumbiro chake cha kwa atate Abrahamu,<\/p>\n<p>Choti timtumikire osa\u0175aopa \u2019dani athu,<br \/>\nNdi kuyeranso mtima mwa chilungamo nsiku zonse.<\/p>\n<p>Mwana, adzakuyesa mneneritu wa Wamkulukulu,<br \/>\nNdiwe udzakonzera njira ya Mbuye Wakumwamba.<\/p>\n<p>Udzadzi\u0175itsa anthu za Mpulumutsi wawo yemwe<br \/>\nA\u0175akhululukira<br \/>\nNafafaniza tchimo lawo,<\/p>\n<p>Poti Mulungu wathu ali ndi mtima wachifundo.<br \/>\nNdiye kumwamba komwe<br \/>\nAtionetsa mbanda kucha,<\/p>\n<p>Po\u0175alitsira omwe ali mumdima ndi muimfa,<br \/>\nNdi potilunjikitsa tonse munjira yamtendere.<\/p>\n","protected":false},"excerpt":{"rendered":"<p>Chichewa Christian Hymns Hymn 28 AMBUYE ngwodalitsika, &nbsp; AMBUYE ngwodalitsika, Mulungu wa Israyeli ndiye, Poti anayang\u2019ana na\u0175awombola anthu ake, Napulumutsa tonse mwapfuko la Davide mwana wake; Monga analankhula mwa aneneri ake, Adzatipulumutsa kudzanja la onse akutida, Ndipo adzachitira akulu chifundo ndi chisoni. Ndiye akumbukira pangani loyera lake lija, Ndi chilumbiro chake cha kwa atate Abrahamu, [&hellip;]<\/p>\n","protected":false},"author":1,"featured_media":0,"comment_status":"open","ping_status":"open","sticky":false,"template":"","format":"standard","meta":{"footnotes":""},"categories":[115],"tags":[],"class_list":["post-3753","post","type-post","status-publish","format-standard","hentry","category-chichewa-christian-hymns"],"amp_enabled":true,"_links":{"self":[{"href":"https:\/\/treasurehymns.com\/nya\/wp-json\/wp\/v2\/posts\/3753","targetHints":{"allow":["GET"]}}],"collection":[{"href":"https:\/\/treasurehymns.com\/nya\/wp-json\/wp\/v2\/posts"}],"about":[{"href":"https:\/\/treasurehymns.com\/nya\/wp-json\/wp\/v2\/types\/post"}],"author":[{"embeddable":true,"href":"https:\/\/treasurehymns.com\/nya\/wp-json\/wp\/v2\/users\/1"}],"replies":[{"embeddable":true,"href":"https:\/\/treasurehymns.com\/nya\/wp-json\/wp\/v2\/comments?post=3753"}],"version-history":[{"count":0,"href":"https:\/\/treasurehymns.com\/nya\/wp-json\/wp\/v2\/posts\/3753\/revisions"}],"wp:attachment":[{"href":"https:\/\/treasurehymns.com\/nya\/wp-json\/wp\/v2\/media?parent=3753"}],"wp:term":[{"taxonomy":"category","embeddable":true,"href":"https:\/\/treasurehymns.com\/nya\/wp-json\/wp\/v2\/categories?post=3753"},{"taxonomy":"post_tag","embeddable":true,"href":"https:\/\/treasurehymns.com\/nya\/wp-json\/wp\/v2\/tags?post=3753"}],"curies":[{"name":"wp","href":"https:\/\/api.w.org\/{rel}","templated":true}]}}