Site icon Treasure Hymns – Chichewa

Hymn 96 MTIMA wanga uyamiketu,

Chichewa Christian Hymns

Hymn 96 MTIMA wanga uyamiketu,

 

MTIMA wanga uyamiketu,
Mfumu yangayo ya Kumwambako;
Mtima wanga uyamiketu,
Zokoma zake za Yesu.

Yesu, Yesu, Yesu,
Inu nokhadi;
Ndikuyamikani,
Ambuye wa moyotu.

Ndiyamike Yesu wangayo,
Anandifera anawukanso;
Andipempherera M’mwambamo,
Abweranso kutenga ‘ne.

Exit mobile version