Site icon Treasure Hymns – Chichewa

Hymn 400 ONA Mwana wa Nkhosa,

Chichewa Christian Hymns

Hymn 400 ONA Mwana wa Nkhosa,

 

ONA Mwana wa Nkhosa,
Ona Mwana wa Nkhosa:
Ona Mwana wa Nkhosa,
Ona Mwana wa Nkhosa.

Malipiro a tchimo,
Ndi imfa yosathayo;
Malipiro a tchimo,
Ndi imfa yosathayo.

Ubadwe mwatsopano,
Ubadwe mwatsopano;
Ubadwe mwatsopano,
Mwa Yesu Ambuyeyo.

Konzeka mbale wanga,
Kukumana ndi Yesu;
Konzeka mbale wanga,
Kukumana ndi Yesu.

Exit mobile version