Chichewa Christian Hymns
Hymn 331 NDILI ndi kwathu ine,
NDILI ndi kwathu ine,
Kumwamba kowalako;
Komwe angelo ayimba,
Ndili ndi kwathu ine.
(M) Kosamangika ndi manja,
(O) Ndi manja,
(M) Kwathu
(O) Kwathuko,
(M) Kokongolako
(O) Kokongolako,
Komwe angelo ayimba
Ndili ndi kwathu ine.
Ndili ndi kwathu ine,
Kumene ndikakhale;
Komwe angelo ayimba,
Ndili ndi kwathu ine.
Ndili ndi kwathu ine,
Kosasinthika konse;
Komwe angelo ayimba,
Ndili ndi kwathu ine.
