Site icon Treasure Hymns – Chichewa

Hymn 318 TINALI ambiri ife,

Chichewa Christian Hymns

Hymn 318 TINALI ambiri ife,

 

TINALI ambiri ife,
Enatu anatisiya;
Chisoni mumtima mwanga.

Amayi, abambo, apita,
Anyamata, atsikana, apita;
Chisoni mumtima mwanga.

Bwera mbale wangawe,
Msangatu kwa Mbuye wako;
Chisoni mumtima mwanga.

Zoipa za m’dziko lino,
Zikusokeretsa anthu;
Chisoni mumtima mwanga.

Bweratu mbale wangawe,
Utsate Ambuye Yesu;
Upeze moyo wosatha.

Exit mobile version