Site icon Treasure Hymns – Chichewa

Hymn 290 NAMONDWE wawuka,

Chichewa Christian Hymns

Hymn 290 NAMONDWE wawuka,

 

NAMONDWE wawuka,
Pakati panyanja;
Tiwoloke bwanji,
Kupita kutsidya;
Yesu ayitana,
Tikamvere Mawu.

(M) Akhrisitu mukupita kuti?
(O) Tikupita kutsidya,
Kutsidya la nyanja.
Yesu ayitana tikamvere Mawu.

Namondwe wauka,
Pakati panyanja;
Tiwoloke bwanji,
Kupita kutsidya;
Yesu analetsa,
Namondwe panyanja.

Namondwe wawuka,
Pakati panyanja;
Tiwoloke bwanji,
Kupita kutsidya;
Yesu alonjeza,
Kutiwolotsatu.

Exit mobile version