Chichewa Christian Hymns
Hymn 217 CHIPULUMUTSO chathu chayandika,
CHIPULUMUTSO chathu chayandika,
Padziko lapansi;
Lapa msanga nthawi yako yatha,
Moyo wako uthanso.
(M) Inetu, sindine ndekha,
(O) Tawomboledwa;
(M) Inetu, sindine ndekha,
(O) Tawomboledwa;
Ngakhale,
Nyanja ndi dziko,
Zonsezi zawomboledwa.
Kodi mbale wanga uchedweranji?
Padziko lapansi;
Fulumira nthawi yako yatha,
Moyo wako uthanso.
Yesu ndiye pothawiratu. ife,
Padziko lapansi;
Lapa msanga nthawi yako yatha,
Moyo wako uthanso.
