Site icon Treasure Hymns – Chichewa

Hymn 211 TIDZALAKALAKA kuwonana naye,

Chichewa Christian Hymns

Hymn 211 TIDZALAKALAKA kuwonana naye,

 

TIDZALAKALAKA kuwonana naye,
Monga Zakeyu anawonana naye;
Tidzalakalaka kuwonana naye,
Mwana wa Mulunguyo.

(Tidzalakalaka) kuwonana naye,
(Tidzalakalaka) kuwonana naye;
(Tidzalakalaka) kuwonana,
Naye, naye, Mbuye.

Ngatitu tifuna kuwonana naye,
Tingomupatsatu mitima yathuyi;
Adzatipatsatu moyo wosathawo,
Moyo wamuyayawo.

Tiyeni tipereke mitima yathu,
Kwa Ambuye wathuyo wa Kumwambako;
Adzatipatsatu moyo wosathawo,
Moyo wamuyayawo.

Exit mobile version