Site icon Treasure Hymns – Chichewa

Hymn 2 YEHOVA Mthandizi,

Chichewa Christian Hymns

Hymn 2 YEHOVA Mthandizi,

 

YEHOVA Mthandizi,
Wamoyo wanga pamavuto;
Amene muchotsa mantha,
Panthawi ya masautso.

Mufungatira moyotu wanga,
Panthawi ya masautso;
Mugwiritsitsa mzimutu wanga,
Panthawi ya masautso.

Yehova Mthandizi,
Wamoyo wanga poyesedwa;
Amene muchotsa mantha,
Panthawi ya masautso.

Yehova Mthandizi,
Wamoyo wanga pomwalira;
Amene muchotsa mantha,
Polowa m’dzenje la imfa.

Exit mobile version