Chichewa Christian Hymns
Hymn 19 MULUNGU akhale nawo,
MULUNGU akhale nawo,
Ulemerero ndi dalitso;
Ndiye Atate, Mwana,
Mzimu Woyera,
Mlungu mmodzi.
Tsopano, poyamba paja,
Masiku onse alinkudza;
Mphamvu, ulemerero,
Dalitso, chipambano.
MULUNGU akhale nawo,
Ulemerero ndi dalitso;
Ndiye Atate, Mwana,
Mzimu Woyera,
Mlungu mmodzi.
Tsopano, poyamba paja,
Masiku onse alinkudza;
Mphamvu, ulemerero,
Dalitso, chipambano.