Site icon Treasure Hymns – Chichewa

Hymn 19 MULUNGU akhale nawo,

Chichewa Christian Hymns

Hymn 19 MULUNGU akhale nawo,

 

MULUNGU akhale nawo,
Ulemerero ndi dalitso;
Ndiye Atate, Mwana,
Mzimu Woyera,
Mlungu mmodzi.

Tsopano, poyamba paja,
Masiku onse alinkudza;
Mphamvu, ulemerero,
Dalitso, chipambano.

Exit mobile version