Site icon Treasure Hymns – Chichewa

Hymn 187 UFUNA kuwomboledwa kodi?

Chichewa Christian Hymns

Hymn 187 UFUNA kuwomboledwa kodi?

 

UFUNA kuwomboledwa kodi?
llipo mphamvu m’ mwazi wake;
Ufuna kugonjetsa zoipa?
Muli mphamvu m’mwazi wake.

Muli mphamvu yodabwitsatu,
M’muazi wa Yesuyo;
Muli mphamuu yodabwvitsatu,
Mmwazi wa Mwanawankhosa.

Ufuna kuleka kunyadako?
Ilipo mphamvu m’mwazi wake;
Idzatu pa mtanda nutsukidwe,
Muli mphamvu m’mwazi wake.

Ufuna kuyera kopambana?
Ilipo mphamvu m’mwazi wake;
Zoipa zonse adzayeretsa,
Muli mphamvu m’mwazi wake.

Ufuna kugwira ntchito yake?
Ilipo mphamvu m’mwazi wake:
Ufuna kumuyimbira lye,
Muli mphamvu m’mwazi wake.

Exit mobile version