Site icon Treasure Hymns – Chichewa

Hymn 114 NDIPO Eliya anati kwa Elisa:

Chichewa Christian Hymns

Hymn 114 NDIPO Eliya anati kwa Elisa:

 

NDIPO Eliya anati kwa Elisa:
“Ukhale pano ndipita ku Beteli.”
Ndipo Elisa anati kwa Eliya:
“Sindidzakusiyani.”

Ndipo Eliya anati kwa Elisa:
“Upemphe chimene ndidzakuchitira.”
Ndipo Elisa anati kwa Eliya:
“M’ndipatse Mzimu wanu.”

Ndipo Eliya anali munthu mnzathu,
Nanga mbalewe uchedwera chiyani;
Sintha mtima ukhale ngati Elisa,
Udzapulumutsidwa.

Exit mobile version