Site icon Treasure Hymns – Chichewa

Hymn 971 Ndinu Mbusa wanga;

Chichewa Believers Christian Hymns

Hymn 971 Ndinu Mbusa wanga;

 

Ndinu Mbusa wanga;

Mndithandizetu;

Ndisaipse nazo

Mtima wangawu.

Osaoopa konse,

Osachimwa ‘yi.

Mndiyendetse Yesu

M’njira yanuyi.

Exit mobile version