Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 970 Pena kumwa nawo,
Pena kumwa nawo,
Ndisateroko,
Pena kukaona
Gule woipa,
Pena kuwombeza
Sindifuna ‘yi;
Yesu mndithandize
Kuzikanazi.
Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 970 Pena kumwa nawo,
Pena kumwa nawo,
Ndisateroko,
Pena kukaona
Gule woipa,
Pena kuwombeza
Sindifuna ‘yi;
Yesu mndithandize
Kuzikanazi.