Site icon Treasure Hymns – Chichewa

Hymn 952 Ndimayenda paulendo,

Chichewa Believers Christian Hymns

Hymn 952 Ndimayenda paulendo,

 

Ndimayenda paulendo,

Ndi yaminga njira yake;

Tsoka ndikapeza, koma

Ndinka kwa Atate;

Pena m’mtima mwanga mwada,

Pena andibvuta ‘dani,

Ndikatenga nkhawa, mantha,

Amadziwako.

Exit mobile version