Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 952 Ndimayenda paulendo,
Ndimayenda paulendo,
Ndi yaminga njira yake;
Tsoka ndikapeza, koma
Ndinka kwa Atate;
Pena m’mtima mwanga mwada,
Pena andibvuta ‘dani,
Ndikatenga nkhawa, mantha,
Amadziwako.
Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 952 Ndimayenda paulendo,
Ndimayenda paulendo,
Ndi yaminga njira yake;
Tsoka ndikapeza, koma
Ndinka kwa Atate;
Pena m’mtima mwanga mwada,
Pena andibvuta ‘dani,
Ndikatenga nkhawa, mantha,
Amadziwako.