Site icon Treasure Hymns – Chichewa

Hymn 936 Ukatha moyo wanga

Chichewa Believers Christian Hymns

Hymn 936 Ukatha moyo wanga

 

Ukatha moyo wanga

Kumwamba kundichera;

Dzuwalo ndimalira

Lafika lokomera.

Usiku m’nali mdima,

Tsopano mbanda kucha;

Kudzawalitsa ndithu

Ku Dziko la Mulungu.

Exit mobile version