Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 936 Ukatha moyo wanga
Ukatha moyo wanga
Kumwamba kundichera;
Dzuwalo ndimalira
Lafika lokomera.
Usiku m’nali mdima,
Tsopano mbanda kucha;
Kudzawalitsa ndithu
Ku Dziko la Mulungu.
Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 936 Ukatha moyo wanga
Ukatha moyo wanga
Kumwamba kundichera;
Dzuwalo ndimalira
Lafika lokomera.
Usiku m’nali mdima,
Tsopano mbanda kucha;
Kudzawalitsa ndithu
Ku Dziko la Mulungu.