Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 917 Ndi nkhondo ikaleka
Ndi nkhondo ikaleka
Kwa Mulungu komweko,
Ndi ukapolo watha,
Udani wathanso;
Ndi zakuopsa zonse
Ndi zosauka zii!
Ndi mwayi wa kwa Mlungu
Udzaza mutu tho!
Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 917 Ndi nkhondo ikaleka
Ndi nkhondo ikaleka
Kwa Mulungu komweko,
Ndi ukapolo watha,
Udani wathanso;
Ndi zakuopsa zonse
Ndi zosauka zii!
Ndi mwayi wa kwa Mlungu
Udzaza mutu tho!