Site icon Treasure Hymns – Chichewa

Hymn 90 Ufuna kuleka kunyadako?

Chichewa Believers Christian Hymns

Hymn 90 Ufuna kuleka kunyadako?

 

Ufuna kuleka kunyadako?

Ilipo mphamvu m’mwazi wake;

Idzatu pa mtanda nutsukidwe,

Muli mphamvu m’mwazi wake.

Exit mobile version