Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 863 A! maliro m’Mpingo mwanu kulirira ‘balewo
A! maliro m’Mpingo mwanu kulirira ‘balewo
Adasokerera kale ndi zoipa zapa dziko.
Muwabwezerenso kwanu kuti akakhale mommo.
Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 863 A! maliro m’Mpingo mwanu kulirira ‘balewo
A! maliro m’Mpingo mwanu kulirira ‘balewo
Adasokerera kale ndi zoipa zapa dziko.
Muwabwezerenso kwanu kuti akakhale mommo.