Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 861 Mbuye, Mpingo wanu usauka kwa kukuludi;
Mbuye, Mpingo wanu usauka kwa kukuludi;
Kale lija munatsitsa Mzimu wanu Wakuyera;
Lero linonso muchite, ulimbike Mpingo wanu.
Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 861 Mbuye, Mpingo wanu usauka kwa kukuludi;
Mbuye, Mpingo wanu usauka kwa kukuludi;
Kale lija munatsitsa Mzimu wanu Wakuyera;
Lero linonso muchite, ulimbike Mpingo wanu.