Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 779 Yesu Mbuye wanga,
Yesu Mbuye wanga,
Mkhale m’mtima mwanga,
Ndiwotu kachisi wanu.
Ikafika imfa,
Mundisunge kwanu
Kuli Inu ndi angelo.
Moyo wanga ulimbike
Kufikira ine
Ndidzakupenyani.
Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 779 Yesu Mbuye wanga,
Yesu Mbuye wanga,
Mkhale m’mtima mwanga,
Ndiwotu kachisi wanu.
Ikafika imfa,
Mundisunge kwanu
Kuli Inu ndi angelo.
Moyo wanga ulimbike
Kufikira ine
Ndidzakupenyani.