Site icon Treasure Hymns – Chichewa

Hymn 779 Yesu Mbuye wanga,

Chichewa Believers Christian Hymns

Hymn 779 Yesu Mbuye wanga,

 

Yesu Mbuye wanga,

Mkhale m’mtima mwanga,

Ndiwotu kachisi wanu.

Ikafika imfa,

Mundisunge kwanu

Kuli Inu ndi angelo.

Moyo wanga ulimbike

Kufikira ine

Ndidzakupenyani.

Exit mobile version