Site icon Treasure Hymns – Chichewa

Hymn 730 A! Yesu mwapangana

Chichewa Believers Christian Hymns

Hymn 730 A! Yesu mwapangana

 

A! Yesu mwapangana

Ndi anthu anuwo

Adzakhala ndinu

Ku Dziko lanulo;

Inenso ndapangana

Ndisabwerere ‘yi;

Mndipatse mphamvu yanu

Ambuye ndinudi.

Exit mobile version