Site icon Treasure Hymns – Chichewa

Hymn 69 Kwathu sipadziko, ndingopitirira,

Chichewa Believers Christian Hymns

Hymn 69 Kwathu sipadziko, ndingopitirira,

 

Kwathu sipadziko, ndingopitirira,

Ndadzikundikira chumaKumwambako;

Mngelo akodola pakhomo lam’mwamba;

Ndipo dziko lapansi sindyesa kwathu.

Exit mobile version