Site icon Treasure Hymns – Chichewa

Hymn 689 Anapeza Mwana

Chichewa Believers Christian Hymns

Hymn 689 Anapeza Mwana

 

Anapeza Mwana

Ali m’kholamo,

Namgwadira Iwo

Mbuye wawoyo;

Anthu onse omwe

Ali pansipa,

Azitsata Mbuye

Ndi nyenyeziyo.

Exit mobile version