Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 689 Anapeza Mwana
Anapeza Mwana
Ali m’kholamo,
Namgwadira Iwo
Mbuye wawoyo;
Anthu onse omwe
Ali pansipa,
Azitsata Mbuye
Ndi nyenyeziyo.
Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 689 Anapeza Mwana
Anapeza Mwana
Ali m’kholamo,
Namgwadira Iwo
Mbuye wawoyo;
Anthu onse omwe
Ali pansipa,
Azitsata Mbuye
Ndi nyenyeziyo.