Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 629 Tinayenda muli mdima
Tinayenda muli mdima
Wotidetsa nkhawawo,
Pena tinangosauka
Ndi zobvuta zathuzo;
Koma Inu munalimo
Mumitambo yomweyo,
Nafe tinathandizana
Ndi mdalitso wanuwo.
Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 629 Tinayenda muli mdima
Tinayenda muli mdima
Wotidetsa nkhawawo,
Pena tinangosauka
Ndi zobvuta zathuzo;
Koma Inu munalimo
Mumitambo yomweyo,
Nafe tinathandizana
Ndi mdalitso wanuwo.