Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 610 Nafenso tidzadzuka kwa ‘ke ngati maluwawo,
Nafenso tidzadzuka kwa ‘ke ngati maluwawo,
Timlambire Mbuye;
Oyera mtima adzabvala mbuu! Pakudza Kristuyo,
Timgwadiretu.
Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 610 Nafenso tidzadzuka kwa ‘ke ngati maluwawo,
Nafenso tidzadzuka kwa ‘ke ngati maluwawo,
Timlambire Mbuye;
Oyera mtima adzabvala mbuu! Pakudza Kristuyo,
Timgwadiretu.