Site icon Treasure Hymns – Chichewa

Hymn 562 Mwa ubwana wake wonse

Chichewa Believers Christian Hymns

Hymn 562 Mwa ubwana wake wonse

 

Mwa ubwana wake wonse

Anakula m’mtima phee!

Anakonda, anafatsa,

Amay’ wake namvabe;

Ndipo ana nonsenu,

Mukamtsate bwinotu.

Exit mobile version