Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 525 Afike masiku
Afike masiku
akuti anthu onse
Adzamva mawu anu
ndi kutsata inu nokha;
Muwale mtima mwawomo,
Adziwe muwakondanso;
Kopani anthu abwere kwa Inu,
Kopani anthu abwere kwa Inu.
Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 525 Afike masiku
Afike masiku
akuti anthu onse
Adzamva mawu anu
ndi kutsata inu nokha;
Muwale mtima mwawomo,
Adziwe muwakondanso;
Kopani anthu abwere kwa Inu,
Kopani anthu abwere kwa Inu.