Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 522 Akazi anadza
Akazi anadza
kwa Yesu ndi anawo,
Anawaletsa anyamata
nawakana ndithu;
Ambuye nawapezadi,
Anati: “Musatero ‘yi,
Lolani ana abwere kwa Ine,
Lolani ana abwere kwa Ine.
Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 522 Akazi anadza
Akazi anadza
kwa Yesu ndi anawo,
Anawaletsa anyamata
nawakana ndithu;
Ambuye nawapezadi,
Anati: “Musatero ‘yi,
Lolani ana abwere kwa Ine,
Lolani ana abwere kwa Ine.