Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 514 Osanatu, osana,
Osanatu, osana,
‘Naimba anawo;
M’kachisi wa Mulungu
Mwamveka nyimboyo.
‘Nalemekeza Yesuyo
Wak’wadalitsayo;
Anamuyamikira
M’ubwana wawowo.
Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 514 Osanatu, osana,
Osanatu, osana,
‘Naimba anawo;
M’kachisi wa Mulungu
Mwamveka nyimboyo.
‘Nalemekeza Yesuyo
Wak’wadalitsayo;
Anamuyamikira
M’ubwana wawowo.