Site icon Treasure Hymns – Chichewa

Hymn 514 Osanatu, osana,

Chichewa Believers Christian Hymns

Hymn 514 Osanatu, osana,

 

Osanatu, osana,

‘Naimba anawo;

M’kachisi wa Mulungu

Mwamveka nyimboyo.

‘Nalemekeza Yesuyo

Wak’wadalitsayo;

Anamuyamikira

M’ubwana wawowo.

Exit mobile version