Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 420 Mtima umabisala
Mtima umabisala
M’manja mwa Yesumu;
Mbuye, musunge ine,
Munandifera ‘ne.
Ndilinda mopirira
Mpaka wachoka mdima.
Ndikaonana naye
Yesu Ambuye wanga.
Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 420 Mtima umabisala
Mtima umabisala
M’manja mwa Yesumu;
Mbuye, musunge ine,
Munandifera ‘ne.
Ndilinda mopirira
Mpaka wachoka mdima.
Ndikaonana naye
Yesu Ambuye wanga.