Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 42 Masiku tikatsala ife
Masiku tikatsala ife
M’dziko mwathu momwe
Mulungu watipatsa ntchito,
Tikazigwiritse.
Pamene zakuipa zathu
Zisautsa ife,
Tikapemphera Mbuye wathu
Atipulumutse.
Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 42 Masiku tikatsala ife
Masiku tikatsala ife
M’dziko mwathu momwe
Mulungu watipatsa ntchito,
Tikazigwiritse.
Pamene zakuipa zathu
Zisautsa ife,
Tikapemphera Mbuye wathu
Atipulumutse.