Site icon Treasure Hymns – Chichewa

Hymn 42 Masiku tikatsala ife

Chichewa Believers Christian Hymns

Hymn 42 Masiku tikatsala ife

 

Masiku tikatsala ife

M’dziko mwathu momwe

Mulungu watipatsa ntchito,

Tikazigwiritse.

Pamene zakuipa zathu

Zisautsa ife,

Tikapemphera Mbuye wathu

Atipulumutse.

Exit mobile version