Site icon Treasure Hymns – Chichewa

Hymn 319 Koma zina sizinadziwa ayi,

Chichewa Believers Christian Hymns

Hymn 319 Koma zina sizinadziwa ayi,

 

Koma zina sizinadziwa ayi,

Makwawa ‘napyola ‘ye,

ndi mdima woopsa wa usikuwo

Ambuye nailonda yake.

Anamva kulira kutaliko,

Naipeza yofoka, yakufayo.

Exit mobile version