Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 317 Zambiri zagona m’kholamo,
Zambiri zagona m’kholamo,
Zosungika bwino ‘mo;
Koma imodzi inasokeradi,
Nitayika m’thengomo
Kutali kuphiri loopsalo,
Kutali ndi mbusa wakeyo.
Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 317 Zambiri zagona m’kholamo,
Zambiri zagona m’kholamo,
Zosungika bwino ‘mo;
Koma imodzi inasokeradi,
Nitayika m’thengomo
Kutali kuphiri loopsalo,
Kutali ndi mbusa wakeyo.