Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 271 Pomwalira Mbuyeyo
Pomwalira Mbuyeyo
Anapfuula kokweza
Naitana Atate
Kupereka mzimu wake;
“Mlungu wanga, Mlungu wanga,
Mwandisiy’ranjitu Ine,
Mundikweze m’Mwambamo,
Landirani mzimu wanga.”
Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 271 Pomwalira Mbuyeyo
Pomwalira Mbuyeyo
Anapfuula kokweza
Naitana Atate
Kupereka mzimu wake;
“Mlungu wanga, Mlungu wanga,
Mwandisiy’ranjitu Ine,
Mundikweze m’Mwambamo,
Landirani mzimu wanga.”