Site icon Treasure Hymns – Chichewa

Hymn 271 Pomwalira Mbuyeyo

Chichewa Believers Christian Hymns

Hymn 271 Pomwalira Mbuyeyo

 

Pomwalira Mbuyeyo

Anapfuula kokweza

Naitana Atate

Kupereka mzimu wake;

“Mlungu wanga, Mlungu wanga,

Mwandisiy’ranjitu Ine,

Mundikweze m’Mwambamo,

Landirani mzimu wanga.”

Exit mobile version