Hymn 270 Zoopsya zopambana treasurehymns 6 months ago Chichewa Believers Christian Hymns Hymn 270 Zoopsya zopambana Zoopsya zopambana Zinachitika pamtanda Kuti mdima unadza, Dzuwa linabisikanso. Chinsalucho cha m’kachisi Chinang’ambika pakati, Myala inaswekanso, Dziko linagwedezeka.