Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 270 Zoopsya zopambana
Zoopsya zopambana
Zinachitika pamtanda
Kuti mdima unadza,
Dzuwa linabisikanso.
Chinsalucho cha m’kachisi
Chinang’ambika pakati,
Myala inaswekanso,
Dziko linagwedezeka.
Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 270 Zoopsya zopambana
Zoopsya zopambana
Zinachitika pamtanda
Kuti mdima unadza,
Dzuwa linabisikanso.
Chinsalucho cha m’kachisi
Chinang’ambika pakati,
Myala inaswekanso,
Dziko linagwedezeka.