Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 263 Mulungu wakwezekatu,
Mulungu wakwezekatu,
Mpulumutsi m’dziko lako,
Wakwezekatu Chitetezo
Wabvundikira iwedi,
Mzimu wanga ‘we wafunda,
Lulutiratu moyo wanga.
Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 263 Mulungu wakwezekatu,
Mulungu wakwezekatu,
Mpulumutsi m’dziko lako,
Wakwezekatu Chitetezo
Wabvundikira iwedi,
Mzimu wanga ‘we wafunda,
Lulutiratu moyo wanga.