Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 256 Ndilira, ndilira,
Ndilira, ndilira,
Ndilira Mbuye Yesu wangadi.
Ndaimba ndi kulira ndi kusisima,
Ndimba ndi kulira ndi kusisima,
Ha! Ha! Aleluya!
Ha! Ha! Aleluya!
Mwasiyiranji Ambuye Yesu?
Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 256 Ndilira, ndilira,
Ndilira, ndilira,
Ndilira Mbuye Yesu wangadi.
Ndaimba ndi kulira ndi kusisima,
Ndimba ndi kulira ndi kusisima,
Ha! Ha! Aleluya!
Ha! Ha! Aleluya!
Mwasiyiranji Ambuye Yesu?