Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 248 Pena pakufadi,
Pena pakufadi,
N’kweza m’Mwamba,
Dzuwa ndi nyenyezi
Zitsalira;
Pomwe ndiimbanso,
Ndidza pafupi pa,
Ndidza pafupi pa
Mlungu wanga.
Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 248 Pena pakufadi,
Pena pakufadi,
N’kweza m’Mwamba,
Dzuwa ndi nyenyezi
Zitsalira;
Pomwe ndiimbanso,
Ndidza pafupi pa,
Ndidza pafupi pa
Mlungu wanga.