Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 191 Sindifuna Mbuye wina,
Sindifuna Mbuye wina,
Koma Yesu yekhayo;
Ine ndili munthu wake,
Iye anandigonjetsa
Ndi kukonda kwakeko.
Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 191 Sindifuna Mbuye wina,
Sindifuna Mbuye wina,
Koma Yesu yekhayo;
Ine ndili munthu wake,
Iye anandigonjetsa
Ndi kukonda kwakeko.