Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 1786 Ndikonda Mlungu pomva Mbuye wanga
Ndikonda Mlungu pomva Mbuye wanga
Amva pemphero ndi kulira kwanga,
Namatchereza khutu nditapfuula,
Andithandiza, nandipulumutsa.
Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 1786 Ndikonda Mlungu pomva Mbuye wanga
Ndikonda Mlungu pomva Mbuye wanga
Amva pemphero ndi kulira kwanga,
Namatchereza khutu nditapfuula,
Andithandiza, nandipulumutsa.