Site icon Treasure Hymns – Chichewa

Hymn 1718 Ona chikondi cha Mulungu,

Chichewa Believers Christian Hymns

Hymn 1718 Ona chikondi cha Mulungu,

 

Ona chikondi cha Mulungu,

Ona zoipazo za anthu,

Koma chakula ndi chikondi;

Wapachikidwa Ambuyathu.

Exit mobile version