Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 1558 Wosangalatsa, ine ndikalira
Wosangalatsa, ine ndikalira
Muchotse nsoni, m’mtimamo mudikhe;
Mundigoneke pachifuwa chake
Cha Yesu kuti ndikakondwepo.
Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 1558 Wosangalatsa, ine ndikalira
Wosangalatsa, ine ndikalira
Muchotse nsoni, m’mtimamo mudikhe;
Mundigoneke pachifuwa chake
Cha Yesu kuti ndikakondwepo.