Site icon Treasure Hymns – Chichewa

Hymn 1187 M’mitima mwathu mwakhala mbee!

Chichewa Believers Christian Hymns

Hymn 1187 M’mitima mwathu mwakhala mbee!

 

M’mitima mwathu mwakhala mbee!

Mtanda wamdima wang’ambwa ke!

Panyanjapo pagawanika.

Ndife tipita ku moyo,

Mtima wabwino ndi moyo;

Kumbanda kucha kwa moyo

Kumatiuza za dzuwalo.

Exit mobile version