Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 1163 Tili ndi mtendere
Tili ndi mtendere
Wopambanatu,
Monga ngati mtsinje
Mumitimamo;
Koma mtsinje uno
Umayenda phee,
Nthawi zonse mtima
Nutonthozabe.
Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 1163 Tili ndi mtendere
Tili ndi mtendere
Wopambanatu,
Monga ngati mtsinje
Mumitimamo;
Koma mtsinje uno
Umayenda phee,
Nthawi zonse mtima
Nutonthozabe.