Site icon Treasure Hymns – Chichewa

Hymn 1163 Tili ndi mtendere

Chichewa Believers Christian Hymns

Hymn 1163 Tili ndi mtendere

 

Tili ndi mtendere

Wopambanatu,

Monga ngati mtsinje

Mumitimamo;

Koma mtsinje uno

Umayenda phee,

Nthawi zonse mtima

Nutonthozabe.

Exit mobile version