Site icon Treasure Hymns – Chichewa

Hymn 1081 Ndikabisala mwanu

Chichewa Believers Christian Hymns

Hymn 1081 Ndikabisala mwanu

 

Ndikabisala mwanu

Ndilibe mantha ‘yi;

Ndikasungidwa kwanu

Mumtima muti phee!

Ndi mphamvu yanu yokha

Ndiposa ‘daniwo;

Chifundo chanu Mbuye

Chitchinjirize ‘ne.

Exit mobile version