Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 1081 Ndikabisala mwanu
Ndikabisala mwanu
Ndilibe mantha ‘yi;
Ndikasungidwa kwanu
Mumtima muti phee!
Ndi mphamvu yanu yokha
Ndiposa ‘daniwo;
Chifundo chanu Mbuye
Chitchinjirize ‘ne.
Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 1081 Ndikabisala mwanu
Ndikabisala mwanu
Ndilibe mantha ‘yi;
Ndikasungidwa kwanu
Mumtima muti phee!
Ndi mphamvu yanu yokha
Ndiposa ‘daniwo;
Chifundo chanu Mbuye
Chitchinjirize ‘ne.