Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 1077 Khalatu woyera,
Khalatu woyera,
Dziko laipadi;
Pemphera kolimba
Kwa Yesu Mbuyathu.
Yang’anitsa Yesu
Ndi kumutsatira,
Kuti anthu ena
Aonenso Iye.
Chichewa Believers Christian Hymns
Hymn 1077 Khalatu woyera,
Khalatu woyera,
Dziko laipadi;
Pemphera kolimba
Kwa Yesu Mbuyathu.
Yang’anitsa Yesu
Ndi kumutsatira,
Kuti anthu ena
Aonenso Iye.